@ted.johnes:

Ted Johnes
Ted Johnes
Open In TikTok:
Region: MW
Sunday 23 February 2025 10:55:30 GMT
38023
748
232
133

Music

Download

Comments

belieyankho
BelieYankho :
simudzabweratu kuno ku central mbuli inu
2025-02-24 06:56:25
3
mwaiwawo1
mwaiwawo1 :
uwuwu ndi umbuli a Malawi tikufunika civil education ya mphamvu mwapindula chani pamenepo molo mopanga spend nthawi ku business kut mudyetse family 🤣
2025-02-24 10:14:20
3
morgan.003
morgan.003 :
Malizitsani galasi oloo chifukwa mtima wanga ukuwawabe nkakumbukira imfa ya anthu 8 ija😭😝😂😂😂
2025-02-24 06:39:15
4
user5100816751270
0832499102 :
😂😂😂😂 Achita bwino anolowela kosalowela
2025-02-23 18:08:43
6
user3333752339461
user3333752339461 :
Sizabwino izi tonse ndi a Malawi osagawa dzikoli ayi
2025-02-24 07:44:47
3
zlatan1gad
KidfromAKRON 1GAD🇲🇼 :
This violence is not good , you mean your parties will not come to central region to do compaings , if anything why not waiting to the voting day. Very Unfortunate Malawi akupita kuti.
2025-02-24 04:15:01
1
christian.bunguzu44
Christian Bunguzu :
Umbuli sudzatithera Amalawi 😱😱😱
2025-02-24 07:29:23
1
charity35mu
Charity😍 :
i like it 😂😂😂
2025-02-24 07:34:17
1
harry.yobe
Harry Yobe :
Amangidwe anthu amenewa ndale nzakale izi
2025-02-24 06:24:17
0
queen.elizabeth.th
QUEEN Elizabeth the third :
to say the truth this is not good at all. let ur vote speak on 16th September. 😳😳😳
2025-02-23 17:12:07
10
pililanikhotho
pililan. kkhottho :
Ndipo sanat tiwaswa asayerekedze kulowela kuthyolo tiwanyenyansi
2025-02-23 19:53:27
3
magphiso
NAMALUNGA :
good athu akufuna chimanga osati misokhano
2025-02-24 08:57:06
1
user7661002021966
Frank pesulo :
very good 👍
2025-02-23 17:21:06
1
limbikaniphiri2
limbikaniphiri246 :
Alesi inu tisiya kukupasani chakudya moti muzikalima busy kugenda
2025-02-24 12:21:24
3
gogomijavi0772369023
gogo mijavi3 :
it's not good
2025-02-24 13:48:04
0
camelizormlumbeh1
Gallagher Mlumbe :
nice
2025-02-23 20:49:31
1
kadasanaishm
Ismael SDK :
nde kwatu kumeneko😅
2025-02-24 11:09:55
1
wilfred.benard4
Wilfred Benard :
munakango phelatu za MCP zakezo azikapangila ku Lilongwe komweko koma kufika mbali zinazi tukuphulisani mitu ndi MCP yanuyo 🤣🤣🤣🤣
2025-02-24 08:35:08
1
leniachigaga
Lenie :
ubwino wake enaso akapita ku Lilongwe amakhapidwa sizachilendo ayi
2025-02-24 08:36:30
1
hastingsmagalasi6
Moureen Kapozo :
Peter mumatani inu athu kulilongwe inu nde lelo yapweka chifukwa chokuti galimoto ya chikangawa yaphwanyudwa🤣🤣🤣🤣🤣
2025-02-24 12:38:05
1
blessings3970
Blessings :
well done
2025-02-23 20:19:53
1
user36298693981
Tawina :
Tangomalizani ndikuotcha ngati mmene inagwera ndege kuchikangawa,ndipo mwachita bwino fanz zandibebera 😁😁😁
2025-02-24 19:14:32
0
user6594800342770
Brendabelb :
kumudzi kwanthu kulibe zibwana😂😂
2025-02-24 19:05:51
0
mike.william9771
Mike William :
anthu wodya chitedxe awa akapolo ziathu zosasalima kuzolowela zolandila munakadya chitedxe mpaka 2030 makape boma ndilomweli
2025-02-24 19:25:41
0
adam.kakonsya
Adam Kakonsya :
He has done very well.
2025-02-23 19:22:39
1
To see more videos from user @ted.johnes, please go to the Tikwm homepage.

Other Videos


About